Ukadaulo ndi ukatswiri ndi  yankho ku Chitukuko- Chakwera

President Lazarus Chakwera  wati ukadaulo ndi ukatswiri mwa achinyamata ndiofunika kwambiri pa chitukuko cha dziko la Malawi. Pa chifukwa ichi, Chakwera wati mpofunika kuti maganizidwe akuya  mdziko  muno apatsidwe chilimbikitso chokwanira. Poyankhula pa mwambo okumbukira tsiku la luso ndi kufukula nzeru zozama, ku Bingu International  Convention Centre (BICC) mu mzinda wa Lilongwe, Chakwera  anatchula ma […]

The post Ukadaulo ndi ukatswiri ndi  yankho ku Chitukuko- Chakwera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください