Tithana ndi aliyese ochita m’bindikilo pa Chingeni, Kalinyeke – atero apolisi

Boma kudzera ku nthambi ya polisi, lakaniza a Malawi kukachita m’bindikilo pa Chingeni komaso Kalinyeke pomwe eni magalimoto akumapeleka ndalama akamadutsa ponena kuti kutero ndi kuphwanya malamulo adziko lino. Izi ndimalingana ndichikalata chomwe nthambi ya polisi yatulutsa Lachisanu pa 21 January chomwe wasainira ndi ofalitsa nkhani wankulu wa polisi a James Kadadzera omwe awuza anthu […]

The post Tithana ndi aliyese ochita m’bindikilo pa Chingeni, Kalinyeke – atero apolisi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください

コメントを残す

メールアドレスが公開されることはありません。 が付いている欄は必須項目です