Ngati achotsa Nankhumwa, achotsanso ife – mamembala ang’amba nsalu za DPP

Pomwe masiku akusenderabe kuchitseko kuti dziko lino lichititse chisankho chaka cha mawa chino, chipani cha Democratic Progressive (DPP) chataya ena mwa mavoti ophaipha, kamba koti anthu ena otsatira a Kondwani Nankhumwa, ati nawoso atuluka nchipani ndipo dzuwa lili phwee, ang’amba nsalu za chipanichi.  Lamulungu pa 28 January, 2024, a Nankhumwa omwe posachedwapa pamodzi ndi anzawo […]

The post Ngati achotsa Nankhumwa, achotsanso ife – mamembala ang’amba nsalu za DPP appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください