Mulili wa chikuku wabuka m’boma la Mchinji

Unduna wa za umoyo wati m’boma la Mchinji mwagwa muliri wa matenda a chikuku omwe pano agwira anthu asanu ndi awiri (7) m’bomali. Malingana ndi kalata yomwe wasayinira ndi mkulu wa zaumoyo m’bomali, Dr Yohane Mwale, pakadali pano mulili m’mudzi mwa Mtiwa m’dera la Chamveka, mfumu yayikulu Simphasi wachulukira. Kalatayi ikusonyeza kuti pa 12 April […]

The post Mulili wa chikuku wabuka m’boma la Mchinji appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください