Aphungu adutsitsa chamba

Mpungwepungwe unakula m’nyumba ya malamulo pamene mbali ya boma yavomereza lamulo kuti ulimi wachamba udzilimidwa m’dziko muno. Izi zinadzetsa mpungwepungwe kunyumbayi pamene aphungu achipani chotsutsa cha Democratic Progressive Party (DPP) anati sakugwirizana ndi lamuloli. Izi zinapangitsa aphungu achipanichi kutuluka pa zokambilanazi ati kusonyeza kusakondwa ndi lamulori. Ngakhale aphunguwa anatuluka panja, nyumbayi inavomereza za biloyi ndipo […]

The post Aphungu adutsitsa chamba appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください