Anthu awili afa galimoto litagwera ku phompho

Anthu awili afa ndipo ena avulala pangozi yagalimoto yomwe yachitika lero pamudzi wa Machinga mboma la Dowa munsewu wa Salima-Lilongwe pamene galimoto yomwe anakwera inalephera kukwera chitunda zomwe zinapangitsa kubwerelambuyo mpaka kukagwera ku phompho. Mneneri wa apolisi ya Dowa Alice Sitima watsimikiza za ngoziyi ndipo wati anthu awiri afawa ndi a Mathews Nekhantani a zaka […]

The post Anthu awili afa galimoto litagwera ku phompho appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください