Zina ukamva: Bambo adula mutu wa nkazi ndi mwana kenaka nkudzikhweza

Bambo wa zaka 27 m’boma la Karonga wadabwitsa anthu pomwe wadula mutu wa nkazi komaso mwana wake kenakaso naye nkudzimangilira. Izi ndi malingana ofalitsa nkhani pa polisi ya Karonga a George Mulewa omwe azindikira bamboyu ngati Jonathan Mzumara omwe apha nkazi wawo Mervis Kumwenda komaso mwana wawo Ian Mzumara. A Mulewa ati nkhaniyi yachitika kumayambiliro […]

The post Zina ukamva: Bambo adula mutu wa nkazi ndi mwana kenaka nkudzikhweza appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください