Kunali mkoke mkoke lero mu Tnm Super League pamene anyamata amakudzulana nthenga, kugwalulana zibwano, kuchotsana chimbenene. Uyu ndi tsatanetsane wamomwe lero masewero athera. Mighty Wanderers yalepherana ndi timu ya Bangwe All Stars, ndipo masewero athera 0 kwa 0. Asilikali a Kamuzu Barracks akuntha ndikufinya kholingo anyamata a Civo Service United ndi Zigoli ziwiri kwa chimodzi. […]
The post Yapamphanthidwa ngati wakuba foni appeared first on Malawi 24.