Wophunzira ku sukulu ya anamwino wadzipha

Ndaine Game wa zaka 42, yemwe anali mu chaka chachiwiri ku sukulu ya anamwino ya Malamulo, wadzimangilira lachisanu masana. Apolisi m’boma la Thyolo atsimikiza za imfa ya a Game omwe amaphnzira za mankhwala ku Malamulo. Mkulu wa apolisi, a Francis Chisoti,  wati Game wasiya kalata yofotokoza za kudziphaku. Malingana ndi a Chisoti, Game yemwe ankachokera […]

The post Wophunzira ku sukulu ya anamwino wadzipha appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください