Wayamba kampeni Mutharika, ali pa Njamba mawa lino

Mtsogoleri wa chipani cha DPP, a Peter Mutharika amene owakonda amangoti APM, akuyembekezereka kugwedeza mzinda wa Blantyre mawa lino pa 12 May. A Mutharika amene akhala nthawi osachititsa msonkhano wandale alengeza kuti akhala pa Njamba Freedom Park. Malinga ndi tsamba lawo la Facebook, iwo ati akubwera pa Njamba kuti afotokozere a Malawi mfundo zawo za […]

The post Wayamba kampeni Mutharika, ali pa Njamba mawa lino appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください