Watha basi! Boma la Chakwera lathetsa mlandu wa Chilima

Ngati wina kundendeko amakonzekera kuti tsiku lina adzakhala mesho wa a Saulos Chilima asiyiletu. Milandu yawo yonse ija a boma aithetsa. Tsopano ndi mfulu. Bwalo la milandu lero pa 6 May lavomereza pempho lochoka kwa mkulu oyimba milandu oti milandu ya katangale yokhudza wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino ithe. Izi zili mu chikalata chimene […]

The post Watha basi! Boma la Chakwera lathetsa mlandu wa Chilima appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください