Wanjatidwa kaamba kogwililira mwana wake yemwe ndikumpatsa pathupi

Bambo wina wa zaka 32 zakubadwa akusungidwa mchitokosi cha apolisi ku Monkey-Bay m’boma la Mangochi kaamba komuganizira kuti wakhala akugwililira mwana wake wa zaka 12 mpaka kufika pomupatsa mimba. Alice Sichali yemwe ndi mneneri pa polisi ya Monkey-Bay wati bamboyu dzina lake ndi Moffat Phiri akumusunga mchitokosi kamba koti akumuganizira kuti wakhala akuchita zadama ndi […]

The post Wanjatidwa kaamba kogwililira mwana wake yemwe ndikumpatsa pathupi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください