Wakamang’ala ku bwalo Doro wa Zeze: anandinamizira kuti ndinakwera bus pomwe ine ndinakwera ndege

Kulitu nkhani ku bwalo uku. A Easter Gondwe omwe amatchuka ndi kukamba nkhani pa tsamba lino la Facebook akasumilidwa. Doro wa Zeze ndiye wakamang’ala kuti a Gondwe ndi a ‘hater’ ndipo amamudyola kwabasi. Akufuna abwalo awalipitse. Malinga ndi zikalata za ku bwalo zomwe Malawi24 yaona, a Dorothy Shonga amene nawonso amaziti ndi celebrity komanso ati […]

The post Wakamang’ala ku bwalo Doro wa Zeze: anandinamizira kuti ndinakwera bus pomwe ine ndinakwera ndege appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください