Unduna wati alimi asagulitse chimanga chinakali m’munda

Pomwe pali chiopsezo cha njala yadzaoneni, unduna wa Zamalimidwe walangiza anthu kuti ayesetse kulima chimanga komaso mbewu zina m’madimba ndipo wachenjeza kuti uthana ndi mchitidwe oberana komaso kugulitsa chimanga ndi mbewu zina zisanakhwimitsitse komanso zinakali m’munda. Izi ndi malingana ndi kalata yomwe undunawu watulutsa yomwe wasainira ndi Dickxie Kampani yemwe ndi mlembi mu unduna wa […]

The post Unduna wati alimi asagulitse chimanga chinakali m’munda appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください