Tiyeni konko! sisitimu ya immigration yabwezeretsedwa, ziphaso zatsika mtengo

A Malawi omwe amafuna kuboola mtambo koma anakhudzidwa ndi kusokonekera kwa sisitimu ya nthambi yoona za anthu olowa ndi kutuluka ya DICS, atha kuusa moyo tsopano poti nthambiyi yati yayambiraso kusindikiza komaso yatsitsa mtengo wa ziphaso zoyendera. Sisitimu ya DICS inasokonekera m’mwezi wa January chaka chino ndipo zakhala zikuveka kuti akathyali ena ndi omwe anapanga […]

The post Tiyeni konko! sisitimu ya immigration yabwezeretsedwa, ziphaso zatsika mtengo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください