Thupi la Khansala Kajosolo wa ku Zomba layikidwa m’manda

Thupi la Malemu Khansala Rams Kajosolo wa Ntiya Ward mu Mzinda wa Zomba yemwe adali wachipani cha UTM layikidwa mmanda lero kumudzi kwao ku Mdeka kwa T/A Chigalu Boma la Blantyre. Poyankhula pamwambo woyika m’manda thupili, wofalitsa nkhani kuchipani cha UTM a Felix Njawala adati mtsogoleri wachipachi Saulosi Chilima yemwenso ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko […]

The post Thupi la Khansala Kajosolo wa ku Zomba layikidwa m’manda appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください