Sukulu ya Msika iwomboledwa ndi ophunzira akale pa Mzuzu University

Sukula ya sekondale ya Msiki m’boma la Mzimba ikusimba lokoma potsatira thandizo lokwanira 4.3 miliyoni  lalandira kuchokera kwa ophunzira akale pa sukulu yaukachenjede ya Mzuzu.  Masiku anayi apitawo,  ophunzira akale pa Mzuzu University anadzidzimutsa sukulu ya Msika ndi thandizo la mabuku olemberamo komanso  ndalama zimene zigwire ntchito ngati sukulu fizi kwa ana khumi ndi asanu.  […]

The post Sukulu ya Msika iwomboledwa ndi ophunzira akale pa Mzuzu University appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください