Sitima iyambiraso kuyenda pakati pa Lilongwe ndi Blantyre

Anthu oyenda maulendo a pakati pa Lilongwe ndi Blantyre tsopano adzikhala ndi chisankho cha mayendedwe awo pomwe boma lalengeza kuti maulendo a sitima yapamtunda ayambiraso pakati pa mizinda iwiriyi. Izi ndi malingana ndi nduna yowona za mtengatenga ndi mtokoma a Jacob Hara omwe  anena izi Lolemba munzinda wa Lilongwe. A Hara ati nkhaniyi ikutsatira kukonzedwa […]

The post Sitima iyambiraso kuyenda pakati pa Lilongwe ndi Blantyre appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください