Sindinakumaneko ndi a Chakwera – Kabambe

M’modzi mwa omwe akufuna kudzaimila kudzapikisana nawo  pa mpando wa utsogoleri wa dziko lino kudzela ku chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) a Dalitso Kabambe ati iwo alibe maganizo aliwonse ogwirizana ndi mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera monga akumvekera manong’onong’o kuti akufuna kudzayenda limodzi mu masankho a 2025. Poyankhula mu uthenga wawo wa Chaka […]

The post Sindinakumaneko ndi a Chakwera – Kabambe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください