Shado wa DPP wapatsidwa belo kutsatila kumangidwa kwake atauza anthu kuti asalole MCP kufika ku Phalombe

Pomwe anthu omwe anaononga katundu wa chipani cha DPP ndikuvulaza mamembala ena a chipanichi ku Lilongwe sanamangidwebe mpaka pano, apolisi ku Phalombe dzulo anathila unyolo membala wa chipani cha DPP yemwe akufuna kudzapikisana nawo pa mpando wa phungu kum’mwera kwa bomalo, kamba kouza otsatira chipanichi kuti ku Phalombe ndi kwa DPP ndipo asalore chipani cha […]

The post Shado wa DPP wapatsidwa belo kutsatila kumangidwa kwake atauza anthu kuti asalole MCP kufika ku Phalombe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください