Red Cross yati ipitiriza kufikira anthu omwe akhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi

Bungwe la Malawi Red Cross Society lati lidzipereka kuthandiza anthu omwe akhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi mu chigawo chapakati ndi kumpoto kwa dziko lino chifukwa ndipo lati chiwerengero cha anthu omwe akusowekera thandizo ndi malo okhala ndi chochuluka. Mkulu oyang’anira zochitikita ndi chitukuko cha anthu mu bungweli, Prisca Chisale, ndiye anayankhula izi pamene amagawa zipangizo […]

The post Red Cross yati ipitiriza kufikira anthu omwe akhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください