Mneneri Christopher Phiri wa zaka 40 yemwe ndi mwini utumiki wa Supernatural Embassy ku Mangochi, wagamulidwa kukaseweza jere zaka khumi, mphambu zisanu ndi zinayi (19) kamba koseweretsa malo obisika a mwana wawo wa mkazi wa zaka 16 zomwe akuti zinali ndi kuthekera koti anakatha kugonana naye. Ngakhale Phiri aloza chala mwana wawoyo kuti anachita kuwaputa […]
The post Pulofeti ochita za akuluakulu ndi mwana wake uja wagamulidwa zaka 19 appeared first on Malawi 24.
Moni Malawi 
