Pasapekeze ogulitsa mafuta mu zigubu — yatero MERA

Pamene mafuta agalimoto akupitilira kusowa m’dziko muno, bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) lati anthu onyamula zigubu asaloledwe kugula mafuta pamalo omwetsera mafuta. Mu chikalata chomwe yatulutsa, MERA yati anthu ena akumagula mafuta ambili mu zigubu ndi cholinga chokuti akagulitsenso mafutawo pa mtengo okwera zomwe zikupangitsa kuti mafuta azipitilira kusowa. Malingana ndi bungweli, kugulitsa […]

The post Pasapekeze ogulitsa mafuta mu zigubu — yatero MERA appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください