Palibe kuthawa apa – a bwalo ampanilira Batatawala

Amafuna kutulukira pawindo koma abwalo akamumbwandira. Mulandu wake wa katangale upitilira basi, ndipo akapezeka olakwa Batatawala n’kutheka akasewenza jele. Oganiziridwa pa milandu ingapo ya katangale, a Abdul Karim Batatawala achoka ndi nkhope ya manyazi ku bwalo la milandu dzulo pamene a bwalo alamula kuti mulandu wawo umodzi pa ingapo okhudza katangale upitilirebe. A Batatawala amene […]

The post Palibe kuthawa apa – a bwalo ampanilira Batatawala appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください