Bwalo lozenga milandu ku Balaka lagamula bambo wa zaka 23 zakubadwa, a Thomas Kanyimbo, kugagwira ntchito ya kalavulagaga ku ndende kwa zaka zisanu ndi chimodzi (6) kaamba kopezeka olakwa pa mlandu ogwililira mwana wake omupeza wa zaka zisanu ndi ziwiri (7). Oimira boma pa milandu, Sub Inspector Liston Sabola, adauza bwalo la milandu kuti bamboyu […]
The post Ogwililira mwana wake omupeza agamulidwa kukakhala ku ndende zaka zisanu ndi chimodzi appeared first on Malawi 24.