Obera anthu ponama kuti mankhwala awo amachiza AIDS agamulidwa chindapusa cha K4.9 miliyoni

Bwalo la milandu la Senior Resident Magistrate m’boma la Mangochi, lagamula anthu awiri omwe amabera anthu ndalama pomanama kuti mankhwala omwe amagulitsa amachiza matenda a AIDS kuti alipile chindapusa cha ndalama zokwana K2,450,000 aliyese. Posachedwapa, apolisi m’boma la Mangochi anamanga mayi Mary Saidi a zaka 25 komaso a Molly Kainga powaganizira kuti akhala akubera anthu […]

The post Obera anthu ponama kuti mankhwala awo amachiza AIDS agamulidwa chindapusa cha K4.9 miliyoni appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください