Nthungululu komanso malikhweru ku Balaka: Escom yakonza vuto la magetsi

Kudamveka kufuula mwa chisangalalo pamene azimai adaimba nthungululu komanso malikhweru adamveka pakati pa abambo ndi achinyamata pamene kampani ya Escom imakonza vuto la magetsi lomwe lidali ku Majiga 2 ntauni ya Balaka. Anthu okhala mdelari akhala opanda magetsi kwa mwezi wathunthu malingana ndi kuonongeka kwa makina a Transformer omwe adapsa. Izi akuti zidakhudza kwambiri anthuwa […]

The post Nthungululu komanso malikhweru ku Balaka: Escom yakonza vuto la magetsi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください