Ntchito yomanga zipinda zophunzirira 10 900 za pulayimale yayambika

Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera wakhazikitsa ntchito yomanga zipinda zophunzilira 10,900 komanso malo osinthira 1000 pansi pa ntchito ya MARP. Polankhula pa mwambowu omwe ukuchitikira pa sukulu ya purayimare ya Chikololere Ku Dedza, Dr. Chakwera ati iyi ndi njira yoonetsetsa kuti ana akuphunzilira malo abwino msukulu za dziko lino. Malinga ndi mtsogoleriyu ntchitoyi […]

The post Ntchito yomanga zipinda zophunzirira 10 900 za pulayimale yayambika appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください