Ndale zonyoza sizitereka nsima – Chakwera

Mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus McCarthy Chakwera wati ndi wokhumudwa ndi khalidwe la andale ena amene akulowetsa ndale pa nkhani ya njala yomwe yagwa mdziko muno. Polankhula m’mzinda wa Blantyre pomwe amatsegulira chipatala cha matenda a khansa cha International Blantyre Cancer Centre (IBCC), Chakwera wati akudziwa kuti andale ena adzimudzudzula iye ngati amene wabweretsa […]

The post Ndale zonyoza sizitereka nsima – Chakwera appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください