Mwamva kulira kwa a Malawi bwana – HRDC yayamikira Chakwera

Bungwe lomenyera ufulu la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) layamikira mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera poyankhula zomwe akuti zikusonyeza kumva kulira kwa a Malawi, ndipo HRDC yati uwu ndi utsogoleri omwe a Malawi amawufuna. Potsatira kuchepa mphamvu kwa ndalama ya Kwacha sabata yatha,  lachitatu madzulo a Chakwera anayankhula ku mtundu wa Malawi ndipo […]

The post Mwamva kulira kwa a Malawi bwana – HRDC yayamikira Chakwera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください