Musazinyenge, Kwacha ilibe mphamvu olo pang’ono – nduna ya zachuma

Nduna yowona za chuma a Simplex Chithyola Banda yati anthu ku Malawi kuno asamazinyenge kuti Kwacha inali ndi mphamvu isanagwetsedwe posachedwapa popeza ndalamayi ilibe mphamvu olo pang’ono. A Chithyola amayankhula izi lero ku BICC ku Lilongwe pa msonkhano wa atolankhani. “Takhala tikudzinyenga pomaonetsa ngati ndalama yathu ya Kwacha inali ya mphamvu koma kumeneko kunali kudzinyenga […]

The post Musazinyenge, Kwacha ilibe mphamvu olo pang’ono – nduna ya zachuma appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください