Musawakwezere malipiro – yakuwa mokweza banki yaikulu

Banki yaikulu mdziko muno ya Reserve yalangiza boma la Malawi komanso ma kampani omwe siaboma kuti asakweze malipiro a ogwira ntchito awo nsanga ponena kuti zitha kusokoneza chuma cha dziko lino. Izi zayankhulidwa lero mu mzinda wa Lilongwe komwe akuluakulu a banki yaikulu m’dziko muno ya Reserve anachititsa msonkhano wa atolankhani komwe anafotokoza zambiri zokhudza […]

The post Musawakwezere malipiro – yakuwa mokweza banki yaikulu appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください