Mulandu wa a Bushiri waimitsidwa

Bwalo la milandu ku Lilongwe laimitsa mulandu wa a Shepherd Bushiri komanso mayi akunyumba kwawo a Mary Bushiri omwe akuyankha milandu yomwe adapalamula mdziko la South Africa. Banja la a Busshiri likuyankha milandu yokhudza kuzembetsa ndalama ku South Africa ndipo boma la dzikolo likufuna awiriwa atumizidwe mdzikolo kuti akayankhe milanduyi. Lero mmawa bwalo la milanduli […]

The post Mulandu wa a Bushiri waimitsidwa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください