M’phunzitsi adya ndalama za ophunzira 17 za mayeso a sitandade 8

Ophunzira okwana 17 ochokera pa sukulu ya pulayimale ya Chawe m’boma la Chiradzulu, ali manja m’khosi pomwe zadziwika kuti salemba nawo mayeso a sitandade 8 kamba koti mphunzitsi wina pa sukuluyi anawadyera ndalama yolipilira mayesowa omwe akulembedwa sabata ino. Watsimikiza za nkhaniyi ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Chiradzulu a Cosmas Kagulo omwe azindikira m’phunzitsiyu […]

The post M’phunzitsi adya ndalama za ophunzira 17 za mayeso a sitandade 8 appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください