Wyson Salad wa zaka 18 amumanga ku Balaka pomuganizila kuti anagwirilira mwana wa zaka zitatu. Mneneri wa polisi ya Balaka a Gladson M’bumpha ati izi zinachitika pa 1 September, 2023 ndipo oganizilidwayo, yemwe ndi amalume ake a mwanayo, wamangidwa dzulo. A M’bumpha ati pa 1 September nthawi ya kumasana a Salad omwe amachita bizinesi ya […]
The post Mnyamata wa zaka 18 wamangidwa chifukwa chogwirilira mwana wa zaka zitatu appeared first on Malawi24.