Mnyamata wa zaka 17 azipha poziwombera ndi mfuti kamba kosemphana ndi chibwezi chake

Mnyamata wa zaka 17 Tinasha Mtawali, wadzipha ku Chitipi m’boma la Lilongwe, pa nkhani zomwe zikuganizilidwa kuti ndi za chibwenzi. Mneneri wa polisi ya Lilongwe a Hastings Chigalu wati mnyamatayu adaimbira lamya chibwenzi chake kuchiuza kuti sadzamuonanso. A Chigalu ati ali mkati molankhulana, bwenzi lakelo linamva kuombedwa kwa mfuti ndipo Tinasha adaleka kulankhura. Izi zidapangitsa […]

The post Mnyamata wa zaka 17 azipha poziwombera ndi mfuti kamba kosemphana ndi chibwezi chake appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください