M’malawi ndi ena atatu akunja amangidwa ku South Africa

Apolisi m’dziko la South Africa amanga nzika ya dziko la Malawi ndi anthu ena atatu akunja powaganizira kuti anaba ma galimoto awiri a mtundu wa Toyota Fortuner ndi Mercedes Benz zomwenso amafuna azizembetse kutuluka nazo m’dzikolo. Malingana ndi ofalitsa nkhani za a Polisi ya m’boma la Limpopo, Brigadier Hlulani Mashaba, anthu atatuwa amangidwa kumathelo a […]

The post M’malawi ndi ena atatu akunja amangidwa ku South Africa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください