Mlingo wa madzi mnyanja ya Malawi ukutsika

Patapita nthawi ma bizinezi ambiri atasokonekera mmbali mwa Nyanja ya Malawi kamba kakusefukila kwa madzi, a National Water Resources Authority (NWRA) ati tsopano mlingo wa madzi mu mnyanjayi ukuphwera. Malingana ndi mneneri wa bungweli, a Masozi Kasambala izi zikudza kamba koti mvula yomwe imagwa ku Tanzania komanso mchigawo cha ku mpoto kwa dziko lino ikutsika. […]

The post Mlingo wa madzi mnyanja ya Malawi ukutsika appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください