Mlandu wa Lester Maganga ulowanso mu bwalo mwezi wamawa

Oweluza Milandu ku bwalo lalikulu a Mzondi Mvula apeleka chitsogozo chakuti mulandu wa a Lester Maganga ukhala ndi masiku khumi ndi anayi (14) kuti umvedwe ndipo kuti oganizilidwawa akakhalebe akusungidwa m’manja mwa a chitetezo kufikila mtsogolo.. Mu kumvedwa kwa mulanduwu lero ku bwalo lalikulu mu mzinda Lilongwe a Lester Maganga akana kuti iwo si olakwa […]

The post Mlandu wa Lester Maganga ulowanso mu bwalo mwezi wamawa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください