Mlaka Maliro ang’alura Chakwera mu nyimbo: Ati ulendo wa ku Canaan sitikafika

Woyimba Mlaka Maliro akuti Malawi wasochera pa ulendo wake waku Canaan kotero sitikafika kamba koti ndodo yotisogolera yasowa. A Maliro awuza atolankhani izizi atawafunsa kuti anenepo pa nyimbo yomwe ayimba koma sinatulusidwe kaye. Mu nyimbo iyi, yotchedwa ndodo, a Maliro akuti: Yasowa, yasowa, yasowa mama ndodoya Moses. Ulendoopitaku Canaan, wavuta tikupita ku Libya. Mama yasowa! […]

The post Mlaka Maliro ang’alura Chakwera mu nyimbo: Ati ulendo wa ku Canaan sitikafika appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください