Mipingo ku Zomba yachita ziwonetsero zodana ndimathanyula

Mipingo yosiyanasiyana motsogodzedwa ndi mpingo wa Katolika Lachinayi yachita ziwonetsero zodana ndimaukwati amuna komanso akazi okhaokha (mathanyula) mu mzinda wa Zomba. Ku zionetserozi kudafika anthu ambiri ndipo zidayambira pa bwalo la Zomba kudzera ku St Charles Lwanga mpaka kukafika kuma office a Bwana Mkubwa (DC) wa Boma la Zomba komwe adakapereka chikalata chamadandaulo awo. Poyankhula […]

The post Mipingo ku Zomba yachita ziwonetsero zodana ndimathanyula appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください