MEC yalimbikitsa anthu a Ntiya Ward kuti adzaponye voti

M’modzi wa makomishonala a bungwe lomwe limawona zachisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) a Caroline Mfune apempha anthu a mdera la Ntiya Ward mu Mzinda wa Zomba kuti adzaponye voti yosankha Khansala wa kumtima kwawo pachisankho chomwe chikuyembekezeka kudzachitika pa 26 September chaka chino. A Mfune adayankhula izi mu Mzinda wa Zomba pomwe […]

The post MEC yalimbikitsa anthu a Ntiya Ward kuti adzaponye voti appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください