Mboni zambali ya Boma zatsiliza kuperekera umboni pamulandu wa a Bon Kalindo

Mboni zisanu zambali ya Boma zatsiliza kuperekera umboni pamulandu wamkulu wa Bungwe la Malawi First a Bon Kalindo omwe akuwayimba mulandu owaganizira kuti adayambitsa zipolowe potsatira ziwonetsero zomwe adachititsa pa 23 November mu mzinda wa Zomba. Zina mwambonizo ndi apolisi anayi omwe ndi Stella Likukuta, Harry Dongolosi, Inspector Gauti, komanso Assistant Superintendent Isaac Mdala. Onsewa […]

The post Mboni zambali ya Boma zatsiliza kuperekera umboni pamulandu wa a Bon Kalindo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください