Mbava zathyola ofesi ya Chilima ku Lilongwe

Apolisi mu mzinda wa Lilongwe ati akusakasaka atsizinamtole omwe athyola ofesi ya wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima ku Capital Hill ku Lilongwe momwe akuti abamo bisiketi ndi inki ya “printer”. A Salome Zgambo omwe ndi ofalitsa nkhani ku polisi ya Lingadzi munzindawu, awuza nyumba zina zofalitsa nkhani mdziko muno kuti akuganizira […]

The post Mbava zathyola ofesi ya Chilima ku Lilongwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください