Mbava inatsakamuka kudenga komwe inabisala apolisi atathira utsi wokhetsa misonzi

Apolisi kwa Jenda akusunga mchitokosi njonda ina yazaka 33 zakubadwa yomwe inapezeka itabisala kudenga la sitolo ndipo anachita kuthira utsi wokhetsa misonzi kuti itsakamukeko. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Macfarlen Mseteka, njondayi yomwe dzina lake ndi Alex Tembo inalowa mu sitolomo yotchedwa Chikwendene Distributors Shop. Njondayi ikuba ndalama inapanga phokoso lomwe alonda anamva. […]

The post Mbava inatsakamuka kudenga komwe inabisala apolisi atathira utsi wokhetsa misonzi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください