Mayi wasiya mwana obadwa kumene pa chipatala cha Salima

Mayi wina  wasiya mwana wongobadwa kumene pa chipata cholowera pa chipatala chachikulu cha boma la Salima mbandakucha wa lero. Mneneri wa a polisi m’boma la Salima a Rabecca Ndiwate wati apolisi Apolisi ku Salima akufunafuna mayiyu. A Ndiwate ati mlonda yemwe amgwira ntchito ya usiku pachipatapo anamva mwana akulira chapafupi ndi pomwe iye anali ndipo […]

The post Mayi wasiya mwana obadwa kumene pa chipatala cha Salima appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください