Mayi wamangidwa kamba kogwilirira mwana wazaka 16

Mayi wazaka 38 yemwe dzina lake ndi Takondwa Banda ali m’manja mwa a polisi ku Kasungu kogwirira mwana wammuna wazaka 16 ndi kumupatsila matenda opatsilana pogonana. Mneneri wa polisi ya Kasungu Joseph Kachikho wati izi zinachitika mu mwezi wa Okotabala chaka chino. A Kachikho ati mnyamatayu analembedwa ntchito yogwira kumunda kwa a Banda ndipo amagona […]

The post Mayi wamangidwa kamba kogwilirira mwana wazaka 16 appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください