Mapemphero anasokonekera ku Lunzu wansembe atathira bakera kwaya masitala

Zachitikanso lero mumpingo wakatolika ku Lunzu pamene wansembe wathira bakera kukamwa oyambitsa kwaya kamba koyambitsa nyimbo ya Aleluya mu nyengo ino ya lenti mpaka mapemphero kusokonekera. Nkhani yonse ikuti a Edward omwe ndi oyambitsa kwaya amene amenyedwawa anayambitsa nyimbo panthawi yopereka mphatso ndipo nyimbo ili mkati panadzamveka mawu oti Aleluya. Apa wansembeyo anadzambatuka ndikukathira bakera […]

The post Mapemphero anasokonekera ku Lunzu wansembe atathira bakera kwaya masitala appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください