Mankhwala a chifuwa chachikulu cha TB ndi aulere – atero adindo

Mpakana pano, anthu ena amaona ngati mankhwala amatenda a chifuwa chachikulu cha TB ndi ogulitsa zinthu zomwe adindo ati zakhala zikupangitsa ena mwa anthu odwala matendawa kuti asamalandire mankhwala mwandondomeko yoyenera komanso kusapita kolandira mankhwala kumene. Izi zadziwika pamene bungwe la African Institute for Development Policy (AFIDEP) mogwirizana ndi bungwe la Journalists Association Against AIDS […]

The post Mankhwala a chifuwa chachikulu cha TB ndi aulere – atero adindo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください