Malipoti akuti Nankhumwa akubwela ndi chake chipani: PDP

Nonse othodwa ndi zipani zonse zilipo pano, ena chabe ongokhala okondwa ndi bambo Kondwani Nankhumwa ndipo mumafunitsitsa atalamula dziko lino, musataye mtima kwenikweni. Chipani chatsopano chikubwela. Okamba akuti ndi cha a Kondwani Nankhumwa. Dzina lake ndi PDP, People’s Development Party. Malinga ndi Malipoti amene Malawi24 yamvetsedwa, ma mulumuzana ena amene anali a chipani cha DPP […]

The post Malipoti akuti Nankhumwa akubwela ndi chake chipani: PDP appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください